Vote For This Song

Lyrics

Undimamatile Lyrics (Verse 1) Usamakhumudwe dzikoli ndi choncho, usamafooke Moyowu ndi choncho, kulakwirana sikulephera, kususulana sikukanika mchikondi, chofunika undigwiritse undikakamile, Chofunika undigwiritse usagive msanga... (Hook) Ndimakukonda, Ndimakufiiila, nchifukwa chake ndinena..Undima..ma..ma..ma..ma..ma..ma..ma..ma..ma..ma..mati..lirebe iwe..Undima..ma..ma..ma..ma..ma..ma..mati..lirebe iwe eeeh.. Undimamatile ndikumamatile Undimamatile ndikumama.. mamamamatilebe iwee...Tikafika.... (Verse 2) Pena ndimalakwitsa kukulakwira mnzangawe Pena ndimachita zodzikonda kukuswerako mtima, koma.. kulakwirana sikulephera, kususulana sikukanika mchikondi.. Chofunika undigwiritse undikakamile Chofunika undigwiritse usagive msanga...(back to chorus) (Bridge) Undimamatile ndikumamatile Undimamatile ndikumama..mamamama... undimaaaaaaaa, Ndikumaaaaaaa...,.

Songwriters

Astabo, OBK

Sharing is cool

You may also like...



Mobile Site

To view this page on the Malawi-Music.com mobile site Click here

Review

Comments
Hits 411 Plays. | 609 Downloads.

Follow Malawi Music on Instagram