Vote For This Song

Lyrics

Intro: Nesnes uuu yeah Chorus: Chikondi koma ichichi Chikondi koma ichichi Chikondi koma ichichi Chikondi koma ichichi Ndili nawe nawe oooh my baby yeah yeah Ndili nawe nawe oooh my baby yeah yeah Ndili nawe nawe Londolondo Ndili nawe nawe Londolondo Ndili nawe nawe Londolondo Londolondo Verse 1: Ndakusowa ndangotumiza ka pic Mtima mwa ine sizakupangamo delete Ndimakondwa umadziwa chikondi ndi awiri Oti sokoneza timamupasa ma kick Oh baby mwetululila olo utaseka Kiki Osatifunila zabwino ameneyo ndi mtiti Chorus Verse 2: Ndimangokonda iwe basi palibe wina Mami sizakusiya ine Mami mpaka ndizayikidwe pansi Ndimangokonda iwe basi palibe wina Mami sizakusiya ine Mami mpaka ndizayikidwe pansi Oh chikondi chathu sichingathe chili Pa repeat Bwela tiyende shosholo tigwetse ma hope Likiti Chorus Bridge: Oooh my baby yeah yeah ndili nawe nawe Oooh my baby yeah yeah ndili nawe nawe Oooh my baby yeah yeah ndili nawe nawe Londolondo Oooh my baby yeah yeah ndili nawe nawe Londolondo Oooh my baby yeah yeah Chorus

Songwriters

Nesnes

Sharing is cool

You may also like...



Mobile Site

To view this page on the Malawi-Music.com mobile site Click here

Review

Comments
Hits 9170 Plays. | 10504 Downloads.

Follow Malawi Music on Instagram