Vote For This Song

Lyrics

Verse 1 Anzanga a age anga pano anakwatira// ­anapeleka phaa nkazi anawanyanyalira//­ anasiya geri nkuyamba ma gobo// wez penda penda pano zikuyenda bhobho.. Anzanga ah age yanga ena Ali pa vep// ife tikadali jobless koma sitiluza faith// mwayi ulipobe ngat sinatipeze death//­ Timangopempha jah jah ationjezele strength.. Anzanga Ena kugeri sanali magenius// Koma pano anaiphula akuyendera ma hirux// omwe tinkakhozafe umphawi watiyanja // Timagulitsa Zibwente kuti tidyese banja.. ah life ndichoncho//Pena zimayenda pena kugwera kumphopho// uzasutha one day sungangokhala pompo//­ osapanga phuma zizayera opanda sopo// Verse 2 Ungokhala ngat tsokonombweee// utha ntunda nkudupha ndukuuza tsokonombwe/ ­umafuna kuphura mwachangu ulowa nazo umbanda// yesa mahaso angapo sachezelera nyimbo imodz mganda.. Mulungu anakupasani.chuma kuti muthandize opelewedwa// malo motithandiza mpameneso tikubeledwa//­ Mdaliso wa mulungu mwasandusa chotilangira// ndife atsokonombwe pano one day muzatigwadira Osaiwala Kuthamanga sikufika malume// njalezo ndizanu koma chuma ndi mbalume// tizapaka chitosi pomwe muzatilume// mano azavunda simuzadya nao beef yothira wa mame.. Koma...aah life ndichoncho//Pena zimayenda pena kugwera kumphopho// uzasutha one day sungangokhala pompo//­ osapanga phuma zizayera opanda sopo.

Sharing is cool

You may also like...



Mobile Site

To view this page on the Malawi-Music.com mobile site Click here

Review

Comments
Hits 24519 Plays. | 58550 Downloads.

Follow Malawi Music on Instagram